Masalimo 34:10 - Buku Lopatulika10 Misona ya mkango isowa nimva njala, koma iwo akufuna Yehova sadzasowa kanthu kabwino. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Misona ya mkango isowa nimva njala, koma iwo akufuna Yehova sadzasowa kanthu kabwino. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Ngakhale anaamkango amasoŵa chakudya ndipo amakhala anjala, koma anthu amene amalakalaka Chauta, sasoŵa zinthu zabwino. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Mikango itha kulefuka ndi kumva njala koma iwo amene amafunafuna Yehova sasowa kanthu kalikonse kabwino. Onani mutuwo |