Masalimo 34:12 - Buku Lopatulika12 Munthu wokhumba moyo ndani, wokonda masiku, kuti aone zabwino? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Munthu wokhumba moyo ndani, wokonda masiku, kuti aone zabwino? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Ndani mwa inu amakhumba moyo ndi kulakalaka kuti akhale masiku ambiri, kuti asangalale ndi zinthu zabwino? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Aliyense wa inu amene amakonda moyo wake ndi kukhumba kuti aone masiku abwino ambiri, Onani mutuwo |