Masalimo 34:13 - Buku Lopatulika13 Uletse lilime lako lisatchule zoipa, ndipo milomo yako isalankhule chinyengo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Uletse lilime lako lisatchule zoipa, ndipo milomo yako isalankhule chinyengo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Ngati ufunadi moyo, usalankhule zoipa, pakamwa pako pasakambe zonyenga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 asunge lilime lake ku zoyipa ndi milomo yake kuti isayankhule zonama. Onani mutuwo |