Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Miyambo 7:1 - Buku Lopatulika

1 Mwananga, sunga mau anga, ukundike malangizo anga,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

1 Mwananga, sunga mau anga, ukundike malangizo anga,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

1 Mwana wanga, mvera mau anga, malamulo anga akhale chuma chako.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

1 Mwana wanga, mvera mawu anga; usunge bwino malamulo angawa.

Onani mutuwo Koperani




Miyambo 7:1
16 Mawu Ofanana  

Landira tsono chilamulo pakamwa pake, nuwasunge maneno ake mumtima mwako.


Mwananga, tamva mwambo wa atate wako, ndi kusasiya chilangizo cha amai ako;


Anzeru akundika zomwe adziwa; koma m'kamwa mwa chitsiru muononga tsopano lino.


Mwananga, usaiwale malamulo anga, mtima wako usunge malangizo anga;


Asachoke kumaso ako; uwasunge m'kati mwa mtima wako.


Mayendedwe ake atsikira kuimfa; mapazi ake aumirira kumanda;


Mwananga, sunga malangizo a atate wako, usasiye malamulo a mai ako;


Sadzalabadira chiombolo chilichonse, sadzapembedzeka ngakhale uchulukitsa malipo.


Koma Iye anati, Inde, koma odala iwo akumva mau a Mulungu, nawasunga.


Ndipo zija za m'nthaka yokoma, ndiwo amene anamva mau nawasunga mu mtima woona ndi wabwino, nabala zipatso ndi kupirira.


Yesu anayankha nati kwa iye, Ngati wina akonda Ine, adzasunga mau anga; ndipo Atate wanga adzamkonda, ndipo tidzadza kwa iye, ndipo tidzayesa kwa iye mokhalamo.


Kumbukirani mau amene Ine ndinanena kwa inu, Kapolo sali wamkulu ndi mbuye wake. Ngati anandilondalonda Ine, adzakulondalondani inunso; ngati anasunga mau anga, adzasunga anunso.


koma temberero, ngati simudzamvera malamulo a Yehova Mulungu wanu, ndi kupatuka m'njira ndikuuzani lero lino, kutsata milungu ina imene simunaidziwa.


Wodala iye amene awerenga, ndi iwo amene akumva mau a chinenerocho, nasunga zolembedwa momwemo; pakuti nthawi yayandikira.


Ndipo ananena kwa ine, Tapenya, usachite; ndine kapolo mnzako, ndi mnzao wa abale ako aneneri, ndi wa iwo akusunga mau a buku ili; lambira Mulungu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa