Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 43:2 - Buku Lopatulika

Ndipo panali pamene atatha kudya tirigu yense anatengayo ku Ejipito atate wao anati kwa iwo, Pitaninso, mukatigulire ife chakudya pang'ono.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo panali pamene atatha kudya tirigu yense anatengayo ku Ejipito atate wao anati kwa iwo, Pitaninso, mukatigulire ife chakudya pang'ono.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tsono banja la Yakobe lija litadya tirigu yense amene adaakasuma ku Ejipito uja, Yakobe adauza ana ake aja kuti, “Pitaninso, mukatigulireko chakudya pang'ono.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Tsono atatha kudya tirigu yense amene anakatenga ku Igupto, Yakobo anati kwa ana ake aja, “Pitani kuti mukatigulire chakudya china pangʼono.”

Onani mutuwo



Genesis 43:2
11 Mawu Ofanana  

Ndipo njala inakula m'dzikomo.


Mfumu, tinatsikira ndithu nthawi yoyamba kudzagula chakudya:


Ndipo Yuda ananena ndi iye kuti, Munthu uja anatilimbitsira mau kuti, simudzaonanso nkhope yanga, koma mphwanu akhale ndi inu ndiko.


Ngati mudzatuma mphwathu pamodzi ndi ife, tidzatsikira ndi kugulira inu chakudya.


Ndipo atate wathu anati, Mupitenso mutigulire ife chakudya pang'ono.


Zapang'ono, ulikuopa Yehova, zipambana ndi katundu wambiri pokhala phokoso.


Kunyada kutsogolera kuonongeka; mtima wodzikuza ndi kutsogolera kuphunthwa.


Asinkhasinkha za munda, naugula; naoka mipesa ndi zipatso za manja ake.


Koma ngati wina sadzisungiratu mbumba yake ya iye yekha, makamaka iwo a m'banja lake, wakana chikhulupiriro iye, ndipo aipa koposa wosakhulupirira.