Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 42:3 - Buku Lopatulika

Ndipo abale ake a Yosefe khumi anatsikira kukagula tirigu mu Ejipito.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo abale ake a Yosefe khumi anatsikira kukagula tirigu m'Ejipito.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Motero abale ake a Yosefe khumi adanyamuka kupita ku Ejipito kukagula tirigu.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Choncho abale ake khumi a Yosefe anapita kukagula tirigu ku Igupto.

Onani mutuwo



Genesis 42:3
4 Mawu Ofanana  

Nati iwo, Akapolo anu ndife abale khumi, ana aamuna a munthu mmodzi m'dziko la Kanani; ndipo, taonani, wamng'ono ali ndi atate wathu lero; ndipo palibe mmodzi.


Ndipo iye anati, Taonani, ndamva kuti mu Ejipito muli tirigu, mutsikireko mutigulire kumeneko; kuti tikhale ndi moyo, tisafe.


Koma Yakobo sanamtume Benjamini mphwake wa Yosefe, pamodzi ndi abale ake, chifukwa anati, Choipa chingam'gwere iye.


Ndipo ana aamuna a Israele anadza kudzagula mwa iwo amene anadzako, pakuti m'dziko la Kanani munali njala.