Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 42:12 - Buku Lopatulika

Ndipo iye anati kwa iwo, Iai, koma mwadzera kuti muone usiwa wa dziko.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo iye anati kwa iwo, Iai, koma mwadzera kuti muone usiwa wa dziko.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Yosefe adati, “Iyai. Inu mwabwera kudzazonda dziko lathu kuti muwone ngati ndi lofooka.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Iye anawawuza kuti, “Ayi! Inu mwabwera kudzaona pamene palibe chitetezo mʼdziko muno.”

Onani mutuwo



Genesis 42:12
4 Mawu Ofanana  

Tonse tili ana aamuna a munthu mmodzi; tili oona, akapolo anu, sitili ozonda.


Nati iwo, Akapolo anu ndife abale khumi, ana aamuna a munthu mmodzi m'dziko la Kanani; ndipo, taonani, wamng'ono ali ndi atate wathu lero; ndipo palibe mmodzi.


Mudzayesedwa ndi ichi, pali moyo wa Farao, simudzatuluka muno, koma akadze kuno mphwanu ndiko.


Mumdziwa Abinere mwana wa Nere kuti anadza kuti akunyengeni, ndi kuti adziwe kutuluka kwanu ndi kulowa kwanu, ndi kuti adziwe zonse mulikuchita inu.