Genesis 42:15 - Buku Lopatulika15 Mudzayesedwa ndi ichi, pali moyo wa Farao, simudzatuluka muno, koma akadze kuno mphwanu ndiko. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Mudzayesedwa ndi ichi, pali moyo wa Farao, simudzatuluka muno, koma akadze kuno mphwanu ndiko. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Tsono ndikuyesani motere; ndikulumbira kuti pali Farao! Inuyo simuchoka, mpaka mng'ono wanuyo atabwera kuno. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Ndiye ndikuyesani motere: Ine ndikulumbira pali Farao ndithu, inuyo simudzachoka malo ano mpaka wotsirizayo atabwera kuno. Onani mutuwo |