Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 42:14 - Buku Lopatulika

14 Ndipo Yosefe anati kwa iwo, Ndicho chimene ndinakunenani inu, kuti, Ndinu ozonda.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

14 Ndipo Yosefe anati kwa iwo, Ndicho chimene ndinakunenani inu, kuti, Ndinu ozonda.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

14 Koma Yosefe adaŵayankha kuti, “Paja ndanena kale kuti ndinu azondi basi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

14 Yosefe anawawuza kuti, “Ndi momwe ndaneneramo: Inu ndinu akazitape.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 42:14
6 Mawu Ofanana  

Nati iwo, Akapolo anu ndife abale khumi, ana aamuna a munthu mmodzi m'dziko la Kanani; ndipo, taonani, wamng'ono ali ndi atate wathu lero; ndipo palibe mmodzi.


Mudzayesedwa ndi ichi, pali moyo wa Farao, simudzatuluka muno, koma akadze kuno mphwanu ndiko.


Mubisiranji nkhope yanu, ndi kundiyesa mdani wanu?


Wandiyatsiranso mkwiyo wake, nandiyesera ngati wina wa adani ake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa