Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 38:4 - Buku Lopatulika

Ndipo anatenganso pakati, nabala mwana wamwamuna, namutcha dzina lake Onani.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anatenganso pakati, nabala mwana wamwamuna, namutcha dzina lake Onani.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Adatenganso pena pathupi nabala mwana wamwamuna, nkumutcha Onani.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Anatenganso pathupi nabala mwana wa mwamuna ndipo anamutcha Onani.

Onani mutuwo



Genesis 38:4
4 Mawu Ofanana  

Ndipo mwamunayo anadziwa mkazi wake Heva: ndipo anatenga pakati, nabala Kaini, ndipo anati, Ndalandira munthu kwa Yehova.


Ndi ana aamuna a Yuda: Eri, ndi Onani, ndi Sela, ndi Perezi, ndi Zera; koma Eri ndi Onani anafa m'dziko la Kanani. Ndi ana aamuna a Perezi ndiwo Hezironi ndi Hamuli.


Ana a Yuda ndiwo Eri, ndi Onani, ndi Sela; Batisuwa Mkanani anambalira atatu amenewa. Koma Eri mwana woyamba wa Yuda anali woipa pamaso pa Yehova, ndi Iye anamupha.


Ana aamuna a Yuda, ndiwo Eri ndi Onani; ndipo Eri ndi Onani anamwalira m'dziko la Kanani.