Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 38:3 - Buku Lopatulika

3 Ndipo anatenga pakati, nabala mwana wamwamuna, namutcha dzina lake Eri.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

3 Ndipo anatenga pakati, nabala mwana wamwamuna, namutcha dzina lake Eri.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

3 Mkaziyo adatenga pathupi nabala mwana wamwamuna, nkumutcha Ere.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

3 Iye anatenga pathupi, nabala mwana wamwamuna amene anamutcha Eri.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 38:3
3 Mawu Ofanana  

Ndi ana aamuna a Yuda: Eri, ndi Onani, ndi Sela, ndi Perezi, ndi Zera; koma Eri ndi Onani anafa m'dziko la Kanani. Ndi ana aamuna a Perezi ndiwo Hezironi ndi Hamuli.


Ana a Yuda ndiwo Eri, ndi Onani, ndi Sela; Batisuwa Mkanani anambalira atatu amenewa. Koma Eri mwana woyamba wa Yuda anali woipa pamaso pa Yehova, ndi Iye anamupha.


Ana aamuna a Yuda, ndiwo Eri ndi Onani; ndipo Eri ndi Onani anamwalira m'dziko la Kanani.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa