Genesis 38:2 - Buku Lopatulika2 Ndipo Yuda anaona kumeneko mwana wamkazi wa Mkanani dzina lake Suwa: ndipo anamtenga, nalowa kwa iye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndipo Yuda anaona kumeneko mwana wamkazi wa Mkanani dzina lake Suwa: ndipo anamtenga, nalowa kwa iye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Kumeneko Yuda adaonako mtsikana Wachikanani, mwana wa Suwa, namkwatira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Kumeneko, Yuda anaona mwana wamkazi wa munthu wina wa Chikanaani wotchedwa Suwa. Anamukwatira nagona naye malo amodzi. Onani mutuwo |