Genesis 38:1 - Buku Lopatulika1 Ndipo panali nthawi yomweyo, kuti Yuda anatsikira kwa abale ake nalowa kwa Mwadulamu, dzina lake Hira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ndipo panali nthawi yomweyo, kuti Yuda anatsikira kwa abale ake nalowa kwa Mwadulamu, dzina lake Hira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Nthaŵi imeneyo Yuda adachoka nakakhala kwa munthu wina wa fuko la Adulamu dzina lake Hira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Pa nthawi imeneyi, Yuda anasiyana ndi abale ake napita kukakhala ndi munthu wina wa ku Adulamu wotchedwa Hira. Onani mutuwo |