Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 38:4 - Buku Lopatulika

4 Ndipo anatenganso pakati, nabala mwana wamwamuna, namutcha dzina lake Onani.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Ndipo anatenganso pakati, nabala mwana wamwamuna, namutcha dzina lake Onani.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Adatenganso pena pathupi nabala mwana wamwamuna, nkumutcha Onani.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Anatenganso pathupi nabala mwana wa mwamuna ndipo anamutcha Onani.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 38:4
4 Mawu Ofanana  

Ndipo mwamunayo anadziwa mkazi wake Heva: ndipo anatenga pakati, nabala Kaini, ndipo anati, Ndalandira munthu kwa Yehova.


Ndi ana aamuna a Yuda: Eri, ndi Onani, ndi Sela, ndi Perezi, ndi Zera; koma Eri ndi Onani anafa m'dziko la Kanani. Ndi ana aamuna a Perezi ndiwo Hezironi ndi Hamuli.


Ana a Yuda ndiwo Eri, ndi Onani, ndi Sela; Batisuwa Mkanani anambalira atatu amenewa. Koma Eri mwana woyamba wa Yuda anali woipa pamaso pa Yehova, ndi Iye anamupha.


Ana aamuna a Yuda, ndiwo Eri ndi Onani; ndipo Eri ndi Onani anamwalira m'dziko la Kanani.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa