Genesis 38:4 - Buku Lopatulika4 Ndipo anatenganso pakati, nabala mwana wamwamuna, namutcha dzina lake Onani. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Ndipo anatenganso pakati, nabala mwana wamwamuna, namutcha dzina lake Onani. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Adatenganso pena pathupi nabala mwana wamwamuna, nkumutcha Onani. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Anatenganso pathupi nabala mwana wa mwamuna ndipo anamutcha Onani. Onani mutuwo |