Genesis 38:5 - Buku Lopatulika5 Ndipo anabalanso mwana wamwamuna, namutcha dzina lake Sela: ndipo iye anali pa Kezibu pamene mkazi anambala iye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Ndipo anabalanso mwana wamwamuna, namutcha dzina lake Sela: ndipo iye anali pa Kezibu pamene mkazi anambala iye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Adabalanso mwana wina wamwamuna, namutcha Sela. Pamene Sela ankabadwa, nkuti Yuda ali ku Kezibu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Anaberekanso mwana wina wamwamuna ndipo anamutcha Sela. Ameneyu anabadwa Yuda ali ku Kezibi. Onani mutuwo |