Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 38:3 - Buku Lopatulika

Ndipo anatenga pakati, nabala mwana wamwamuna, namutcha dzina lake Eri.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anatenga pakati, nabala mwana wamwamuna, namutcha dzina lake Eri.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Mkaziyo adatenga pathupi nabala mwana wamwamuna, nkumutcha Ere.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Iye anatenga pathupi, nabala mwana wamwamuna amene anamutcha Eri.

Onani mutuwo



Genesis 38:3
3 Mawu Ofanana  

Ndi ana aamuna a Yuda: Eri, ndi Onani, ndi Sela, ndi Perezi, ndi Zera; koma Eri ndi Onani anafa m'dziko la Kanani. Ndi ana aamuna a Perezi ndiwo Hezironi ndi Hamuli.


Ana a Yuda ndiwo Eri, ndi Onani, ndi Sela; Batisuwa Mkanani anambalira atatu amenewa. Koma Eri mwana woyamba wa Yuda anali woipa pamaso pa Yehova, ndi Iye anamupha.


Ana aamuna a Yuda, ndiwo Eri ndi Onani; ndipo Eri ndi Onani anamwalira m'dziko la Kanani.