Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 36:3 - Buku Lopatulika

ndi Basemati mwana wamkazi wa Ismaele, mlongo wake wa Nebayoti.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

ndi Basemati mwana wamkazi wa Ismaele, mlongo wake wa Nebayoti.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

ndi Basemati mwana wa Ismaele, mlongo wa Nebayoti.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

ndi Basemati mwana wa Ismaeli, amenenso anali mlongo wa Nabayoti.

Onani mutuwo



Genesis 36:3
6 Mawu Ofanana  

ndipo maina a ana a Ismaele, maina ao m'mibadwo yao ndi awa: woyamba wa Ismaele ndi Nebayoti; ndi Kedara, ndi Adibeele, ndi Mibisamu,


Pamene Esau anali wa zaka makumi anai, anakwatira Yuditi mwana wamkazi wa Beeri Muhiti, ndi Basemati mwana wamkazi wa Eloni Muhiti.


ndipo Esau ananka kwa Ismaele, naonjezera kwa akazi amene anali nao, natenga Mahalati mwana wamkazi wa Ismaele mwana wa Abrahamu, mlongo wake wa Nebayoti akhale mkazi wake.


amenewa ndi maina a ana aamuna a Esau: Elifazi mwana wamwamuna wa Ada, mkazi wake wa Esau, Reuwele mwana wamwamuna wa Basemati mkazi wake wa Esau.


Esau anatenga akazi ake a ana aakazi a mu Kanani: Ada mwana wamkazi wa Eloni Muhiti, ndi Oholibama mwana wamkazi wa Ana, mwana wamkazi wa Zibiyoni Muhivi;


Ndipo Ada anambalira Esau Elifazi; ndipo Basemati anabala Reuwele;