Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 36:10 - Buku Lopatulika

10 amenewa ndi maina a ana aamuna a Esau: Elifazi mwana wamwamuna wa Ada, mkazi wake wa Esau, Reuwele mwana wamwamuna wa Basemati mkazi wake wa Esau.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

10 amenewa ndi maina a ana amuna a Esau: Elifazi mwana wamwamuna wa Ada, mkazi wake wa Esau, Reuwele mwana wamwamuna wa Basemati mkazi wake wa Esau.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

10 Maina a ana aamuna a Esau naŵa: Elifazi mwana wa Ada mkazi wa Esau, ndi Reuele mwana wa Basemati mkazi wa Esau.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

10 Awa ndi mayina a ana aamuna a Esau: Elifazi, mwana wa Ada, mkazi wa Esau, ndi Reueli, mwana wamwamuna wa Basemati, mkazi wa Esau.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 36:10
5 Mawu Ofanana  

Pamene Esau anali wa zaka makumi anai, anakwatira Yuditi mwana wamkazi wa Beeri Muhiti, ndi Basemati mwana wamkazi wa Eloni Muhiti.


Ndipo ana aamuna a Elifazi ndiwo Temani, Omara, Zefo ndi Gatamu, ndi Kenazi.


Mibadwo ya Esau atate wao wa Aedomu m'phiri la Seiri ndi iyi:


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa