Genesis 36:11 - Buku Lopatulika11 Ndipo ana aamuna a Elifazi ndiwo Temani, Omara, Zefo ndi Gatamu, ndi Kenazi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Ndipo ana amuna a Elifazi ndiwo Temani, Omara, Zefo ndi Gatamu, ndi Kenazi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Ana a Elifazi ndi Temani, Omara, Zefo, Gatamu ndi Kenazi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Awa ndi mayina a ana a Elifazi: Temani, Omari, Zefo, Gatamu ndi Kenazi. Onani mutuwo |