Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 36:11 - Buku Lopatulika

11 Ndipo ana aamuna a Elifazi ndiwo Temani, Omara, Zefo ndi Gatamu, ndi Kenazi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

11 Ndipo ana amuna a Elifazi ndiwo Temani, Omara, Zefo ndi Gatamu, ndi Kenazi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

11 Ana a Elifazi ndi Temani, Omara, Zefo, Gatamu ndi Kenazi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

11 Awa ndi mayina a ana a Elifazi: Temani, Omari, Zefo, Gatamu ndi Kenazi.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 36:11
7 Mawu Ofanana  

amenewa ndi maina a ana aamuna a Esau: Elifazi mwana wamwamuna wa Ada, mkazi wake wa Esau, Reuwele mwana wamwamuna wa Basemati mkazi wake wa Esau.


Ndipo Timna anali mkazi wake wamng'ono wa Elifazi mwana wamwamuna wa Esau; ndipo anambalira Elifazi Amaleke: amenewa ndi ana aamuna a Ada mkazi wake wa Esau.


Atamva tsono mabwenzi atatu a Yobu za choipa ichi chonse chidamgwera, anadza, yense kuchokera kwao, Elifazi wa ku Temani, ndi Bilidadi Msuki, ndi Zofari wa ku Naama, napangana kudzafika kumlirira ndi kumsangalatsa.


Za Edomu. Yehova wa makamu atero: Kodi mu Temani mulibenso nzeru? Kodi uphungu wawathera akuchenjera? Kodi nseru zao zatha psiti?


Ndipo amuna anu amphamvu adzatenga nkhawa, Temani iwe, kuti onse aonongeke m'phiri la Edomu, ndi kuphedwa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa