Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 27:44 - Buku Lopatulika

ukhale naye masiku akuwerengeka, mpaka utamchokera ukali mkulu wako;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

ukhale naye masiku akuwerengeka, mpaka wamchokera ukali wa mkulu wako;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Bakakhala kwa iyeyo kanthaŵi ndithu,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ukakhale naye kwa kanthawi mpaka mkwiyo wa mʼbale wako utatsika.

Onani mutuwo



Genesis 27:44
3 Mawu Ofanana  

Zaka makumi awiriwo ndakhala nawe, nkhosa ndi mbuzi zako zazikazi sizinapoloze, ndi abira a zoweta zako sindinadye.


Ndinakhala chotere zaka makumi awiri m'nyumba mwako; zaka khumi ndi zinai ndinakutumikira iwe chifukwa cha ana ako aakazi awiri, ndi zaka zisanu ndi chimodzi chifukwa cha zoweta zako; wasintha malipiro anga kakhumi.


Pakuti Ambuye Yehova wa makamu ndiye amene akhudza dziko, nilisungunuka; ndi onse okhalamo adzachita maliro; ndipo lidzakwera lonseli ngati madzi a m'mtsinje; nilidzatsikanso ngati mtsinje wa mu Ejipito;