Amosi 9:5 - Buku Lopatulika5 Pakuti Ambuye Yehova wa makamu ndiye amene akhudza dziko, nilisungunuka; ndi onse okhalamo adzachita maliro; ndipo lidzakwera lonseli ngati madzi a m'mtsinje; nilidzatsikanso ngati mtsinje wa mu Ejipito; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Pakuti Ambuye Yehova wa makamu ndiye amene akhudza dziko, nilisungunuka; ndi onse okhalamo adzachita maliro; ndipo lidzakwera lonseli ngati madzi a m'nyanja; nilidzatsikanso ngati nyanja ya m'Ejipito; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Ambuye Chauta Wamphamvuzonse, akakhudza dziko, limanyenyeka, ndipo zonse zokhala m'menemo zimalira. Apo dziko lonse limafufuma ngati mtsinje wa Nailo ndipo limateranso ngati mtsinje wa Nailo wa ku Ejipito. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Ambuye Yehova Wamphamvuzonse amene amakhudza dziko lapansi ndipo dzikolo limasungunuka, onse amene amakhala mʼmenemo amalira. Dziko lonse lidzadzaza ngati mtsinje wa Nailo, kenaka nʼkuphwera ngati mtsinje wa ku Igupto. Onani mutuwo |