Amosi 9:4 - Buku Lopatulika4 Angakhale alowa ndende pamaso pa adani ao, kumeneko ndidzalamulira lupanga, ndipo lidzawapha; ndipo ndidzayang'anitsa maso anga kwa iwowa, kuwachitira choipa, si chokoma ai. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Angakhale alowa ndende pamaso pa adani ao, kumeneko ndidzalamulira lupanga, ndipo lidzawapha; ndipo ndidzayang'anitsa maso anga kwa iwowa, kuwachitira choipa, si chokoma ai. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Ngakhale adani ao aŵakusire ku ukapolo, komweko ndidzalamula kuti aphedwe pa nkhondo. Ndidzaŵayang'anitsitsa kuti ziŵagwere zoipa osati zabwino.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Ngakhale adani awo awakusire ku ukapolo, ndidzalamula lupanga kuti liwaphe kumeneko. Ndidzawayangʼanitsitsa kuti zoyipa ziwagwere; osati zabwino.” Onani mutuwo |