Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 27:34 - Buku Lopatulika

Pamene Esau anamva mau a atate wake Isaki, analira ndi kulira kwakukulu ndi kowawa kopambana, nati kwa atate wake, Mundidalitse ine, inenso atate wanga.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pamene Esau anamva mau a atate wake Isaki, analira ndi kulira kwakukulu ndi kowawa kopambana, nati kwa atate wake, Mundidalitse ine, inenso atate wanga.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Esau atamva zimenezi, adalira kwambiri ndi mtima woŵaŵa, ndipo adati, “Bambo, pepani inenso mundidalitseko.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Esau atamva mawu a abambo ake, analira mokweza ndi mowawidwa mtima nati kwa abambo ake, “Inenso dalitseni abambo anga!”

Onani mutuwo



Genesis 27:34
8 Mawu Ofanana  

Ndipo iye anati, Mphwako anadza monyenga, nalanda mdalitso wako.


Koma podziwa Mordekai zonse zidachitikazi, Mordekai anang'amba zovala zake, navala chiguduli ndi mapulusa, natuluka pakati pa mzinda, nafuula, nalira kulira kwakukulu ndi kowawa,


momwemo adzadya zipatso za mayendedwe ao, nadzakhuta zolingalira zao.


Utsiru wa munthu ukhotetsa njira yake; mtima wake udandaula pa Yehova.


Pakuti mudziwa kutinso pamene anafuna kulowa dalitsolo, anakanidwa (pakuti sanapeze malo akulapa), angakhale analifunafuna ndi misozi.


Ndipo Davide ndi anthu amene anali naye anakweza mau ao, nalira misozi, kufikira analibe mphamvu yakuliranso.