1 Samueli 30:4 - Buku Lopatulika4 Ndipo Davide ndi anthu amene anali naye anakweza mau ao, nalira misozi, kufikira analibe mphamvu yakuliranso. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Ndipo Davide ndi anthu amene anali naye anakweza mau ao, nalira misozi, kufikira analibe mphamvu yakuliranso. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Tsono Davide ndi anthu ake adalira mokweza, mpaka mphamvu zolirira zidaŵathera. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Kotero Davide ndi anthu ake analira mofuwula mpaka analibenso mphamvu zolirira. Onani mutuwo |