Genesis 27:35 - Buku Lopatulika35 Ndipo iye anati, Mphwako anadza monyenga, nalanda mdalitso wako. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201435 Ndipo iye anati, Mphwako anadza monyenga, nalanda mdalitso wako. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa35 Koma Isaki adayankha kuti, “Mng'ono wako anabwera, ndipo wandinyenga. Iyeyo ndiye amene watenga madalitso ako onse.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero35 Koma iye anati, “Mʼbale wako anabwera mwachinyengo ndipo watenga madalitso ako.” Onani mutuwo |