Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 27:16 - Buku Lopatulika

ndipo anaveka zikopa za tiana tambuzi pamanja ake ndi pakhosi pake posalala;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

ndipo anaveka zikopa za tiana tambuzi pamanja ake ndi pakhosi pake posalala;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Adamuvekanso zikopa za tianatambuzi pamikono pake ndiponso pakhosi pake posalala popanda cheya.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Anamuvekanso manja ake ndi khosi lake ndi zikopa za mwana wambuzi.

Onani mutuwo



Genesis 27:16
4 Mawu Ofanana  

Ndipo woyamba anabadwa wofiira, mwake monse monga malaya aubweya; ndipo anamutcha dzina lake Esau.


Ndipo Rebeka anatenga zovala zokoma za Esau mwana wake wamkulu zinali m'nyumba, naveka nazo Yakobo mwana wake wamng'ono;


ndipo anapereka m'dzanja la mwana wake Yakobo chakudya chokoleracho, ndi mikate imene anaipanga.


Ndipo sanamzindikire iye, chifukwa kuti manja ake anali aubweya, onga manja a Esau mkulu wake; ndipo anamdalitsa iye.