Genesis 25:25 - Buku Lopatulika25 Ndipo woyamba anabadwa wofiira, mwake monse monga malaya aubweya; ndipo anamutcha dzina lake Esau. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201425 Ndipo woyamba anabadwa wofiira, mwake monse monga malaya aubweya; ndipo anamutcha dzina lake Esau. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa25 Mwana woyamba kubadwa anali wofiira, ndipo thupi lake lonse linali ngati chovala chaubweya. Motero adamutcha Esau. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero25 Woyamba kubadwa anali wofiira, ndipo thupi lake lonse linali ngati chovala cha ubweya; choncho anamutcha Esau. Onani mutuwo |