Genesis 27:15 - Buku Lopatulika15 Ndipo Rebeka anatenga zovala zokoma za Esau mwana wake wamkulu zinali m'nyumba, naveka nazo Yakobo mwana wake wamng'ono; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Ndipo Rebeka anatenga zovala zokoma za Esau mwana wake wamkulu zinali m'nyumba, naveka nazo Yakobo mwana wake wamng'ono; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Pambuyo pake Rebeka adatenga zovala zabwino za Esau zimene ankazisunga m'nyumba, naveka mng'ono wake Yakobe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Tsono Rebeka anatenga zovala zabwino kwambiri za Esau mwana wake wamkulu zimene zinali mʼnyumba namuveka Yakobo. Onani mutuwo |