Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 27:16 - Buku Lopatulika

16 ndipo anaveka zikopa za tiana tambuzi pamanja ake ndi pakhosi pake posalala;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

16 ndipo anaveka zikopa za tiana tambuzi pamanja ake ndi pakhosi pake posalala;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

16 Adamuvekanso zikopa za tianatambuzi pamikono pake ndiponso pakhosi pake posalala popanda cheya.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

16 Anamuvekanso manja ake ndi khosi lake ndi zikopa za mwana wambuzi.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 27:16
4 Mawu Ofanana  

Ndipo woyamba anabadwa wofiira, mwake monse monga malaya aubweya; ndipo anamutcha dzina lake Esau.


Ndipo Rebeka anatenga zovala zokoma za Esau mwana wake wamkulu zinali m'nyumba, naveka nazo Yakobo mwana wake wamng'ono;


ndipo anapereka m'dzanja la mwana wake Yakobo chakudya chokoleracho, ndi mikate imene anaipanga.


Ndipo sanamzindikire iye, chifukwa kuti manja ake anali aubweya, onga manja a Esau mkulu wake; ndipo anamdalitsa iye.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa