Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 27:23 - Buku Lopatulika

23 Ndipo sanamzindikire iye, chifukwa kuti manja ake anali aubweya, onga manja a Esau mkulu wake; ndipo anamdalitsa iye.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

23 Ndipo sanamzindikire iye, chifukwa kuti manja ake anali aubweya, onga manja a Esau mkulu wake; ndipo anamdalitsa iye.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

23 Sadamzindikire Yakobe popeza kuti mikono yake inali yacheya ngati ya Esau. Motero adayambapo kumdalitsa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

23 Sanamuzindikire, popeza mikono yake inali ndi ubweya ngati ya mʼbale wake Esau; choncho anamudalitsa.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 27:23
6 Mawu Ofanana  

Yakobo ndipo anati kwa Rebeka amake, Taonani, Esau mkulu wanga ndiye munthu waubweya, ine ndine munthu wosalala.


ndipo anaveka zikopa za tiana tambuzi pamanja ake ndi pakhosi pake posalala;


Ndipo Yakobo anasendera kwa Isaki atate wake, ndipo anamyambasa nati, Mau ndi mau a Yakobo, koma manja ndi manja a Esau.


Ndipo anati, Kodi ndiwe mwana wanga weniweni Esau? Ndipo anati, Ndine amene.


Ndi chikhulupiriro Isaki anadalitsa Yakobo ndi Esau, zingakhale za zinthu zilinkudza.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa