Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 23:12 - Buku Lopatulika

Ndipo Abrahamu anawerama pamaso pa anthu a m'dzikomo.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Abrahamu anawerama pamaso pa anthu a m'dzikomo.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Apo Abrahamu adaŵerama pamaso pa anthu onse aja,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Apo Abrahamu anaweramanso mwaulemu pamaso pa anthu a mʼdzikolo

Onani mutuwo



Genesis 23:12
5 Mawu Ofanana  

Ndipo anatukula maso ake, nayang'ana, taonani, anthu atatu anaima pandunji pake; pamene anaona iwo, anawathamangira kuchoka ku khomo la hema kukakomana nao, nawerama pansi, nati,


Ndipo anadza ku Sodomu madzulo amithenga awiri; ndipo Loti anakhala pa chipata cha Sodomu, ndipo Loti anaona iwo, nauka kuti akakomane nao, ndipo anaweramitsa pansi nkhope yake.


Iai, mfumu, mundimvere ine; munda ndikupatsani inu, ndi phanga lili m'menemo ndikupatsani inu, pamaso pa ana a anthu anga ndikupatsani inu; ikani wakufa wanu.


Ndipo ananena kwa Efuroni alinkumva anthu a m'dzikomo, kuti, Koma ngati ufuna, undimveretu ine: ndidzakupatsa iwe mtengo wake wa munda; uulandire kwa ine, ndipo ndidzaika wakufa wanga m'menemo.


Ndipo anauka Abrahamu naweramira anthu a m'dzikomo, ana a Hiti.