Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 2:6 - Buku Lopatulika

koma inakwera nkhungu yotuluka padziko lapansi, nkuthirira ponse pamwamba panthaka.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

koma inakwera nkhungu yotuluka pa dziko lapansi, niithirira ponse pamwamba pa nthaka.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Koma madzi ankatuluka m'dziko lonse lapansi ndi kumathirira nthaka.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

koma kasupe ankatuluka mʼnthaka ndi kuthirira pa dziko lonse.

Onani mutuwo



Genesis 2:6
3 Mawu Ofanana  

Ndi zomera zonse za m'munda zisanakhale m'dziko lapansi, ndiponso matherere onse a m'munda asanamere; chifukwa Yehova Mulungu sanavumbitsire mvula padziko lapansi, ndipo panalibe munthu wakulima nthaka;


Ndipo Yehova Mulungu anaumba munthu ndi dothi lapansi, nauzira mpweya wa moyo m'mphuno mwake; munthuyo nakhala wamoyo.


Akweza mitambo ichokere ku malekezero a dziko lapansi; ang'animitsa mphezi zidzetse mvula; atulutsa mphepo mosungira mwake.