Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Genesis 2:6 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

6 koma kasupe ankatuluka mʼnthaka ndi kuthirira pa dziko lonse.

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

6 koma inakwera nkhungu yotuluka padziko lapansi, nkuthirira ponse pamwamba panthaka.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

6 koma inakwera nkhungu yotuluka pa dziko lapansi, niithirira ponse pamwamba pa nthaka.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

6 Koma madzi ankatuluka m'dziko lonse lapansi ndi kumathirira nthaka.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 2:6
3 Mawu Ofanana  

zitsamba zinali zisanamere ndipo chomera chilichonse chinali chisanamerenso popeza Yehova Mulungu anali asanagwetse mvula pa dziko lapansi. Panalibe munthu wolima nthaka,


Tsono Yehova Mulungu anawumba munthu kuchokera ku dothi nawuziramo mpweya wamoyo mʼmphuno mwake ndipo munthuyo anakhala wamoyo.


Iye amatulutsa mitambo kuchokera ku malekezero a dziko lapansi, amatumiza zingʼaningʼani pamodzi ndi mvula ndipo amatulutsa mphepo ku malo ake osungiramo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa