Genesis 2:6 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 koma kasupe ankatuluka mʼnthaka ndi kuthirira pa dziko lonse. Onani mutuwoBuku Lopatulika6 koma inakwera nkhungu yotuluka padziko lapansi, nkuthirira ponse pamwamba panthaka. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 koma inakwera nkhungu yotuluka pa dziko lapansi, niithirira ponse pamwamba pa nthaka. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Koma madzi ankatuluka m'dziko lonse lapansi ndi kumathirira nthaka. Onani mutuwo |