Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 11:16 - Buku Lopatulika

Ndipo Eberi anakhala ndi moyo zaka makumi atatu kudza zinai, nabala Pelegi;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Eberi anakhala ndi moyo zaka makumi atatu kudza zinai, nabala Pelegi;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Eberi ali wa zaka 34, adabereka mwana dzina lake Pelegi.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pamene Eberi anali ndi zaka 34 anabereka Pelegi.

Onani mutuwo



Genesis 11:16
7 Mawu Ofanana  

Ndiponso kwa Semu atate wa ana onse a Eberi, mkulu wa Yafeti, kwa iye kunabadwa ana.


Kwa Eberi ndipo kunabadwa ana aamuna awiri; dzina la wina ndi Pelegi; chifukwa kuti m'masiku ake dziko lapansi linagawanikana; dzina la mphwake ndi Yokotani.


ndipo Sela anakhala ndi moyo zaka mazana anai kudza zitatu, atabala Eberi, nabala ana aamuna ndi aakazi.


ndipo Eberi anakhala ndi moyo zaka mazana anai kudza makumi awiri, atabala Pelegi, nabala ana aamuna ndi aakazi.


Ndi Eberi anabala ana aamuna awiri, dzina la winayo ndiye Pelegi, popeza masiku ake dziko linagawanika; ndi dzina la mbale wake ndiye Yokotani.


Koma zombo zidzafika kuchokera ku dooko la Kitimu, ndipo adzasautsa Asiriya, nadzasautsa Eberi, koma iyenso adzaonongeka.


mwana wa Serugi, mwana wa Reu, mwana wa Pelegi, mwana wa Eberi, mwana wa Sela,