Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 11:15 - Buku Lopatulika

15 ndipo Sela anakhala ndi moyo zaka mazana anai kudza zitatu, atabala Eberi, nabala ana aamuna ndi aakazi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

15 ndipo Sela anakhala ndi moyo zaka mazana anai kudza zitatu, atabala Eberi, nabala ana aamuna ndi aakazi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

15 Pambuyo pake adakhala ndi moyo zaka zina 403, ndipo adaberekanso ana ena aamuna ndi aakazi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

15 Atabereka Eberi, Sela anakhala ndi moyo zaka zina 403 ndipo anali ndi ana ena aamuna ndi aakazi.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 11:15
2 Mawu Ofanana  

Ndipo Sela anakhala ndi moyo zaka makumi atatu, nabala Eberi;


Ndipo Eberi anakhala ndi moyo zaka makumi atatu kudza zinai, nabala Pelegi;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa