Genesis 11:16 - Buku Lopatulika16 Ndipo Eberi anakhala ndi moyo zaka makumi atatu kudza zinai, nabala Pelegi; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Ndipo Eberi anakhala ndi moyo zaka makumi atatu kudza zinai, nabala Pelegi; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Eberi ali wa zaka 34, adabereka mwana dzina lake Pelegi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Pamene Eberi anali ndi zaka 34 anabereka Pelegi. Onani mutuwo |