Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 11:17 - Buku Lopatulika

17 ndipo Eberi anakhala ndi moyo zaka mazana anai kudza makumi awiri, atabala Pelegi, nabala ana aamuna ndi aakazi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

17 ndipo Eberi anakhala ndi moyo zaka mazana anai kudza makumi awiri, atabala Pelegi, nabala ana aamuna ndi aakazi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

17 Pambuyo pake adakhala ndi moyo zaka zina 430, ndipo adaberekanso ana ena aamuna ndi aakazi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

17 Atabereka Pelegi, Eberi anakhala ndi moyo zaka zina 430 ndipo anali ndi ana ena aamuna ndi aakazi.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 11:17
2 Mawu Ofanana  

Ndipo Eberi anakhala ndi moyo zaka makumi atatu kudza zinai, nabala Pelegi;


Ndipo Pelegi anakhala ndi moyo zaka makumi atatu, nabala Reu;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa