Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 11:18 - Buku Lopatulika

18 Ndipo Pelegi anakhala ndi moyo zaka makumi atatu, nabala Reu;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

18 Ndipo Pelegi anakhala ndi moyo zaka makumi atatu, nabala Reu;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

18 Pelegi ali wa zaka 30 adabereka mwana dzina lake Reu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

18 Pamene Pelegi anali ndi zaka makumi atatu, anabereka Reu.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 11:18
3 Mawu Ofanana  

ndipo Eberi anakhala ndi moyo zaka mazana anai kudza makumi awiri, atabala Pelegi, nabala ana aamuna ndi aakazi.


ndipo Pelegi anakhala ndi moyo zaka mazana awiri kudza zisanu ndi zinai, atabala Reu, nabala ana aamuna ndi aakazi.


mwana wa Serugi, mwana wa Reu, mwana wa Pelegi, mwana wa Eberi, mwana wa Sela,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa