Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 11:19 - Buku Lopatulika

19 ndipo Pelegi anakhala ndi moyo zaka mazana awiri kudza zisanu ndi zinai, atabala Reu, nabala ana aamuna ndi aakazi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

19 ndipo Pelegi anakhala ndi moyo zaka mazana awiri kudza zisanu ndi zinai, atabala Reu, nabala ana aamuna ndi aakazi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

19 Pambuyo pake adakhala ndi moyo zaka zina 209, ndipo adaberekanso ana ena aamuna ndi aakazi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

19 Atabereka Reu, Pelegi anakhala zaka zina 209 ndipo anali ndi ana ena aamuna ndi aakazi.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 11:19
2 Mawu Ofanana  

Ndipo Pelegi anakhala ndi moyo zaka makumi atatu, nabala Reu;


Ndipo Reu anakhala ndi moyo zaka makumi atatu kudza ziwiri, nabala Serugi:


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa