Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 11:14 - Buku Lopatulika

14 Ndipo Sela anakhala ndi moyo zaka makumi atatu, nabala Eberi;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

14 Ndipo Sela anakhala ndi moyo zaka makumi atatu, nabala Eberi;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

14 Pamene Sela anali wa zaka 30, adabereka mwana dzina lake Eberi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

14 Pamene Sela anali ndi zaka makumi atatu, anabereka Eberi.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 11:14
2 Mawu Ofanana  

ndipo Aripakisadi anakhala ndi moyo zaka mazana anai kudza zitatu, atabala Sela, nabala ana aamuna ndi aakazi.


ndipo Sela anakhala ndi moyo zaka mazana anai kudza zitatu, atabala Eberi, nabala ana aamuna ndi aakazi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa