Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 11:13 - Buku Lopatulika

13 ndipo Aripakisadi anakhala ndi moyo zaka mazana anai kudza zitatu, atabala Sela, nabala ana aamuna ndi aakazi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

13 ndipo Aripakisadi anakhala ndi moyo zaka mazana anai kudza zitatu, atabala Sela, nabala ana aamuna ndi aakazi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

13 Pambuyo pake adakhala ndi moyo zaka zina 403, ndipo adaberekanso ana ena aamuna ndi aakazi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

13 Atabereka Sela, Aripakisadi anakhala ndi moyo zaka zina 403 ndipo anali ndi ana ena aamuna ndi aakazi.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 11:13
2 Mawu Ofanana  

Ndipo Aripakisadi anakhala ndi moyo zaka makumi atatu kudza zisanu nabala Sela;


Ndipo Sela anakhala ndi moyo zaka makumi atatu, nabala Eberi;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa