Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 10:17 - Buku Lopatulika

ndi Ahivi, ndi Aariki, ndi Asini;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

ndi Ahivi, ndi Aariki, ndi Asini;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ahivi, Aariki, Asini,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ahivi, Aariki, Asini,

Onani mutuwo



Genesis 10:17
6 Mawu Ofanana  

ndi Ayebusi, ndi Aamori, ndi Agirigasi;


ndi Aaravadi, ndi Aazemari, ndi Ahamati; pambuyo pake pamenepo ndipo mabanja a Akanani anafalikira.


Pamene anamuona iye Sekemu, mwana wake wamwamuna wa Hamori Muhivi, kalonga wa dzikolo, anamtenga nagona ndi iye, namuipitsa.


ndi Ahivi, ndi Aariki, ndi Asini,


Ndipo anthu onse otsala mwa Ahiti, ndi Aamori, ndi Aperizi, ndi Ahivi, ndi Ayebusi, osati Aisraele,


Ndipo amuna a Israele anati kwa Ahivi, Kapena mulimkukhala pakati pa ife, ndipo tipanganenji ndi inu?