2 Mbiri 8:7 - Buku Lopatulika7 Ndipo anthu onse otsala mwa Ahiti, ndi Aamori, ndi Aperizi, ndi Ahivi, ndi Ayebusi, osati Aisraele, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ndipo anthu onse otsala mwa Ahiti, ndi Aamori, ndi Aperizi, ndi Ahivi, ndi Ayebusi, osati Aisraele, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Koma analipo anthu ena otsalira a mitundu yosiyanasiyana: Ahiti, Aamori, Aperezi, Ahivi ndi Ayebusi. Ameneŵa sanali Aisraele, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Panali anthu amene anatsala pakati pa mitundu ya Ahiti, Aamori, Aperezi, Ahivi ndi Ayebusi (anthu awa sanali Aisraeli). Onani mutuwo |