Yoswa 9:7 - Buku Lopatulika7 Ndipo amuna a Israele anati kwa Ahivi, Kapena mulimkukhala pakati pa ife, ndipo tipanganenji ndi inu? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ndipo amuna a Israele anati kwa Ahivi, Kapena mulimkukhala pakati pa ife, ndipo tipanganenji ndi inu? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Koma Aisraele adayankha kuti, “Mwina mwake kwanu nkufupi konkuno. Nanga tingachite nanu chipangano bwanji?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Koma Aisraeli anayankha Ahiviwo kuti, “Mwinatu inu mukukhala pafupi ndi ife. Tsono ife tingachite bwanji mgwirizano ndi inu?” Onani mutuwo |