Genesis 34:2 - Buku Lopatulika2 Pamene anamuona iye Sekemu, mwana wake wamwamuna wa Hamori Muhivi, kalonga wa dzikolo, anamtenga nagona ndi iye, namuipitsa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Pamene anamuona iye Sekemu, mwana wake wamwamuna wa Hamori Muhivi, kalonga wa dzikolo, anamtenga nagona ndi iye, namuipitsa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Sekemu, mwana wa Hamori Muhivi, amene anali mfumu ya chigawo cha dzikolo, atamuwona namwaliyo, adamgwira nagona naye. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Pamene Sekemu mwana wa Hamori Mhivi, mfumu ya deralo, anamuona, anamugwirira. Onani mutuwo |