Genesis 34:3 - Buku Lopatulika3 Ndipo mtima wake unakhumba Dina mwana wake wamkazi wa Yakobo, ndipo anamkonda namwaliyo, nanena momkopa namwaliyo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Ndipo mtima wake unakhumba Dina mwana wake wamkazi wa Yakobo, ndipo anamkonda namwaliyo, nanena momkopa namwaliyo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Sekemu ankamukondadi Dina, mwana wa Yakobe, ndipo ankamulankhula mau achikondi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Koma Sekemu anamukondadi namwali uja, Dina, mwana wa Yakobo motero kuti anamuyankhula mawu womutonthoza. Onani mutuwo |
Chifukwa chake tsono nyamukani, mutuluke, nimulankhule zowakondweretsa anyamata anu; pakuti ndilumbira, Pali Yehova, kuti mukapanda kutuluka inu, palibe munthu mmodzi adzakhala nanu usiku uno; ndipo chimenechi chidzakuipirani koposa zoipa zonse zinakugwerani kuyambira ubwana wanu kufikira tsopanoli.