Genesis 34:4 - Buku Lopatulika4 Ndipo anati Sekemu kwa atate wake Hamori kuti, Munditengere ine mkazi uyo akhale mkazi wanga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Ndipo anati Sekemu kwa atate wake Hamori kuti, Munditengere ine mkazi uyo akhale mkazi wanga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Choncho adakauza bambo wake kuti, “Nditengereni namwaliyu kuti akhale mkazi wanga.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Choncho Sekemu anati kwa abambo ake Hamori, “Mundipezere mtsikana uyu kuti akhale mkazi wanga.” Onani mutuwo |