Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 1:23 - Buku Lopatulika

Ndipo panali madzulo ndipo panali m'mawa, tsiku lachisanu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo panali madzulo ndipo panali m'mawa, tsiku lachisanu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tsono kudali madzulo ndiponso m'maŵa, tsiku lachisanu.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndipo panali madzulo ndiponso mmawa pa tsiku lachisanu.

Onani mutuwo



Genesis 1:23
6 Mawu Ofanana  

Mulungu ndipo anadalitsa zimenezo, nati, Zibalane, zichuluke, zidzaze madzi a m'nyanja, ndi mbalame zichuluke padziko lapansi.


Ndipo adati Mulungu, Dziko lapansi libale zamoyo monga mwa mitundu yao, ng'ombe, ndi zokwawa, ndi zinyama za dziko lapansi monga mwa mitundu yao: ndipo kunatero.


Ndipo anaziona Mulungu zonse zimene adazipanga, ndipo, taonani, zinali zabwino ndithu. Ndipo panali madzulo ndipo panali m'mawa, tsiku lachisanu ndi chimodzi.


Ndipo Mulungu anatcha kuyerako Usana, ndi mdimawo anautcha Usiku. Ndipo panali madzulo ndipo panali m'mawa, tsiku loyamba.


Ndipo Mulungu analitcha thambolo Kumwamba. Ndipo panali madzulo ndipo panali m'mawa, tsiku lachiwiri.


Ndipo Yesu ananena naye, Ndithu ndinena ndi iwe, kuti lero, usiku uno, tambala asanalire kawiri, udzandikana Ine katatu.