Genesis 1:22 - Buku Lopatulika22 Mulungu ndipo anadalitsa zimenezo, nati, Zibalane, zichuluke, zidzaze madzi a m'nyanja, ndi mbalame zichuluke padziko lapansi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Mulungu ndipo anadalitsa zimenezo, nati, Zibalane, zichuluke, zidzaze madzi a m'nyanja, ndi mbalame zichuluke pa dziko lapansi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Adazidalitsa ponena kuti, “Swanani ndipo mudzaze nyanja, mbalamenso ziswane pa dziko.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Mulungu anazidalitsa nati, “Muswane, ndi kudzaza mʼmadzi a mʼnyanja, ndipo mbalame zichuluke pa dziko lapansi.” Onani mutuwo |