Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 1:19 - Buku Lopatulika

Ndipo panali madzulo ndipo panali m'mawa, tsiku lachinai.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo panali madzulo ndipo panali m'mawa, tsiku lachinai.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ndipo kudali madzulo ndiponso m'maŵa, tsiku lachinai.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndipo panali madzulo ndiponso mmawa pa tsiku lachinayi.

Onani mutuwo



Genesis 1:19
6 Mawu Ofanana  

zilamulire usana ndi usiku, zilekanitse kuyera ndi mdima: ndipo anaona Mulungu kuti kunali kwabwino.


Ndipo anati Mulungu, Madzi abale zochuluka zamoyo zoyendayenda, ndi mbalame ziuluke pamwamba padziko lapansi ndi pamlengalenga.


Ndipo anaziona Mulungu zonse zimene adazipanga, ndipo, taonani, zinali zabwino ndithu. Ndipo panali madzulo ndipo panali m'mawa, tsiku lachisanu ndi chimodzi.


Ndipo Mulungu anatcha kuyerako Usana, ndi mdimawo anautcha Usiku. Ndipo panali madzulo ndipo panali m'mawa, tsiku loyamba.


Ndipo Mulungu analitcha thambolo Kumwamba. Ndipo panali madzulo ndipo panali m'mawa, tsiku lachiwiri.


Ndipo Yesu ananena naye, Ndithu ndinena ndi iwe, kuti lero, usiku uno, tambala asanalire kawiri, udzandikana Ine katatu.